N
Kuwala kwa Kum’mawa
Mu Mpingo wa Mulungu, Mulungu Atate ndi Mulungu Amayi, Nkumene Kuwala Koona, Kumapezeka
Kuti tidziwe ngati ntchito zathundi zolondola kapena zolakwika,tiyenera kubwera kwa Mulungu,amene ali kuunika koona.
Masiku ano, m’dziko lamdimakumene anthu sangathe kuzindikirachifuniro cha Mulungu,Khristu Ahnsahnghong ndiMulungu Amayi awunikirakuunika kwa chowonadicha moyo kudzera mu Sabata ndi Paska.
Mulungu ndiye kuunika,ndipo ana a Mulungundi ana a kuunika
Mulungu anabwera ku dziko lapansingati kuunika, kugonjetsa mzimuwa dziko la mdima, kutiphunzitsaza zinthu zakumwamba, kubweretsachiyembekezo ku dziko lapansi,ndi kuwalitsa kuunika.Chimodzimodzi, ana aMulungu ayenera kuunikiransokuwala kwa Uthenga Wabwinokudziko lapansi kuti aliyense adziwe Mulungu.
[M]wa amene mulungu wa nthawi ino ya pansi pano anachititsa khungu maganizo ao a osakhulupirira, kuti chiwalitsiro cha Uthenga Wabwino wa ulemerero wa Khristu, amene ali chithunzithunzi cha Mulungu, chisawawalire. . . . Pakuti Mulungu amene anati, Kuunika kudzawala kutuluka mumdima, ndiye amene anawala m’mitima yathu kutipatsa chiwalitsiro cha chidziwitso cha ulemerero wa Mulungu pankhope pa Yesu Khristu.
2 Akorinto 4:4–6
Nambala ya Owonera49
#Mulungu Wobwera M'nthupi
#Mulungu Elohim
#Chipulumutso