Mulungu anakhazikitsa Paska pakukhetsa mwazi wake pa mtanda kuti apulumutse anthu. Mamembala a Mpingo woyambirira adadutsa mchizunzo chachikulu, kukhala chakudya cha mikango ndi zoyikapo nyali za anthu chifukwa adasunga Paska, choonadi cha moyo. Pambuyo pa M’bado wa Atumwi, Paska anathetsedwa mu AD 325 malinga ndi kuumirira kwa Mpingo wa Kumadzulo kupyolera mu Mikangano yosiyanasiyana ya Paska.
Masiku ano, mpingo wa Mulungu umasunga Paska kukhala wopatulika monga mmene mpingo woyamba unkachitira, mosiyana ndi mipingo ina padziko lapansi. Ndi chifukwa chakuti Mpingo wa Mulungu umakhulupirira kwambiri kuti ziphunzitso za Khristu Ahnsahnghong ndi Mulungu Amayi, amene anabwera kudzatipulumutsa, ndi choonadi cha moyo chimene chimapulumutsa anthu ku masoka.
“Ife,” iye anatero, “chifukwa chake timasunga tsiku lenileni; osawonjezerapo kapena kuchotsapo. . . . Onsewa anasunga tsiku lakhumi ndi cinai la Paska monga mwa Uthenga Wabwino, osapatuka konse, koma kutsata lamulo la cikhulupiriro. Komanso, ine, Polycrates, amene ndine wamng’ono wa inu nonse, malinga ndi mwambo wa achibale anga, ena amene ine ndawatsatira.”
119 Bundang P.O.Box, Bundang-gu, Seongnam-si, Gyeonggi-do, Rep. of KOREA
Tel 031-738-5999 Fax 031-738-5998
Likulu la Ofesi: 50, Sunae-ro, Bundang-gu, Seongnam-si, Gyeonggi-do, Dziko la Korea
Mpingo Waukulu: 35, Pangyoyeok-ro, Bundang-gu, Seongnam-si, Gyeonggi-do, Dziko la Korea
ⓒ Gulu la Utumiki wa Dziko Lonse la Mpingo wa Mulungu. Ma Umwini onse ndi Otetezedwa Mfundo za Zinsinsi